Ndimamva kuti kunyamula manja popanga du'aa ndi bid'ah, koma pali ma ahādīth ena ofotokoza za kunyamula manja, nde ndimakhala osokonezeka kwambiri ndi ziwiri zimenezi. Tsopano ndimafuna munditambasulire kuti kodi ndi swalah ziti komanso ndi nthawi ziti zimene zikuloledwa kupanga du'aa utanyamula manja?